Kwa anthu ambiri amene anasonkhana pa malo ochitira msonkhano a Mboni Za Yehova ku Lilongwe ndi ena amene analumikizidwa m’mipingo yosiyanasiyana m’Malawi komanso mayiko oyandikira, June 14, 2026 ndi tsiku limene adzalikumbukira mwapadera popeza analandira mphatso ya Baibulo la Dziko Latsopano m’Chiyao.





















