A Nankhumwa, Jeffrey ndi Ena Awachotsa mu DPP

A Nankhumwa achotsedwa nawo A Nankhumwa achotsedwa nawo

Chipani cha DPP chachotsa m'chipanichi ena mwa akuluakulu ake monga a Kondwani Nankhumwa, a Grezelder Jeffrey, a Mark Botomani, a Nicholas Dausi ndi a Ken Msonda mwa ena.

Malingana ndi kalata yomwe chipanichi chatulutsa Loweruka, izi zadza pumbuyo pa zokambirana zomwe akulu akulu a komiti yosungitsa mwambo m’chipanichi analinazo masiku apitawo ndi adindowa.

Onse omwe awachotsa mu DPP ndi khumi ndi m’modzi.

Koma a Ken Msonda, mmodzi mwa omwe awachotsa, ati zachitikazi ndi zolakwika, ndipo ati mwina kunali bwino anthuwa anakangowayimitsa m’maudindo awo.

Read 2075 times
Login to post comments

NEWS IN BRIEF

Malawians who Abandoned Israeli Farms Deported

The Malawi government says Israel has deported 12 Malawian workers…
Read more...

Last Witness Testifies in Matemba’s Case

The Anti-Corruption Bureau (ACB) has finished parading witnesses in the…
Read more...

Owaganizira Kupha Awamanga

Apolisi amanga abambo atatu - a Gift Banda a zaka…
Read more...

Court Adjourns Chisale’s Case

Principal Resident Magistrate Rodrick Michongwe has adjourned to a later…
Read more...

NBS Yawonjezera Makobili a Chikho

Bank ya NBS lero yalengeza kuti yakweza ndalama zomwe imapereka…
Read more...
Go to top
JSN Time 2 is designed by JoomlaShine.com | powered by JSN Sun Framework