Standard Bank - BOL to Wallet

Loya Wati Athandiza Mayi waku Mchinji Yemwe Apolisi Anamumanga Pamodzi ndi Khanda Lake

Loya wina Alexious Kamangila ,wadzipereka kuti ayimira mwaulere mayi wa zaka 30 ku Mchinji, yemwe wakhala akusungidwa ndi a polisi pamodzi ndi mwana wake pa mlandu wonyanyalira mwamuna khanda.

A Kamangila, omwe ndi mphunzitsi ku univesite ya Malawi, ati atawerenga nkhani ya maiyu pa Zodiak Online aganiza zomuimilira kuti athandizire chilungamo pa nkhaniyi.

A Matilda Chirwa, omwe pano ali pa belo, dzulo anakawonekera ku khothi komwe wachiwiri kwa Magistrate Anne Simwaka wayimitsa mlandu-wu mpaka lachisanu sabata ya mawa pofuna kulola oyimira boma pa mlanduwu kuti abweretse mboni.

Pakadali pano, magistrate Simwaka wagwirizana ndi pempho la loya-yu kuti mayiyu akamuwunike achipatala, ngati kumangidwa kwake sikunasokoneze kaganizidwe kake komanso umoyo wake poti anali atachira chakumene.

Read 4208 times

Last modified on Thursday, 10/08/2023

Login to post comments

NEWS IN BRIEF

Apolisi Amanga Woganiziridwa Kutaya Mwana

Apolisi kwa Ngabu m'boma la Chikwawa amanga mai wa zaka…
Read more...

Rising Suicide: Psychologist Blames Lack on Trust

A top psychologist has blamed the sharp rise in suicide…
Read more...

Tourism Grows as Malawi Launches National Tourism Month

Minister of Tourism Vera Kamtukule says the tourism sector has…
Read more...

Father Boucher Remembered for Preserving Malawian Culture

The departed Catholic priest, father Claude Boucher, has been described…
Read more...

Malawi Chewa Group to Hold Parallel Chifukwato Ceremony

Barely a few days after some the Chewa people led…
Read more...
Go to top
JSN Time 2 is designed by JoomlaShine.com | powered by JSN Sun Framework