Mvula Ipitilira

Nthambi yoona zanyengo m'dziko muno yati palibe nkhawa iliyonse ya ng’amba mwezi uno wa January. 

Mneneri wa nthambiyi, a Yobu Kachiwanda, wanena izi potsatira uthenga omwe akuluakulu azanyengo ku Zimbabwe apereka kwa mzika za dzikolo kuti kukhala ng’amba kuyambira Lachisanu sabata yatha mpaka pa 2 Febuluwale.

A Kachiwanda ati ngakhale maiko a Malawi ndi Zimbabwe amakhala ndi nyengo yofanana, dziko lino lipitilira kulandira mvula ya mlingo wochuluka monga momwe analengezera m’mwezi wa September chaka chatha.

Read 1539 times
Login to post comments

NEWS IN BRIEF

Malawians who Abandoned Israeli Farms Deported

The Malawi government says Israel has deported 12 Malawian workers…
Read more...

Last Witness Testifies in Matemba’s Case

The Anti-Corruption Bureau (ACB) has finished parading witnesses in the…
Read more...

Owaganizira Kupha Awamanga

Apolisi amanga abambo atatu - a Gift Banda a zaka…
Read more...

Court Adjourns Chisale’s Case

Principal Resident Magistrate Rodrick Michongwe has adjourned to a later…
Read more...

NBS Yawonjezera Makobili a Chikho

Bank ya NBS lero yalengeza kuti yakweza ndalama zomwe imapereka…
Read more...
Go to top
JSN Time 2 is designed by JoomlaShine.com | powered by JSN Sun Framework